icekay malawi mbuye amandikonda şarkı sözleri

Intro Afuna nditagwa afuna nditaputwa Afuna nditafa afuna ndingoduwa Pre hook Sindikhala ndimatha Mbuye amandikonda He is always on my side He is always on my side Sindikhala ndimatha Mbuye amandikonda He is always on my side He is always on my side Mbuye wanga kawawa Palibe ofanana naye Iye sanditaya alindicholinga nane Mbuye wanga kawawa Palibe ofanana naye Iye sanditaya alindicholinga nane Hook Dani wanga amafuna ndiduke Ndiyaluke ndiduke Amafuna ndiduke Ndiyaluke ndiduke Dani wanga amafuna ndiduke Ndiyaluke ndiduke Amafuna ndiduke Ndiyaluke ndiduke Verse Ohh Yahwe Ndinu mbambande U always here and u never late Mumandipasa phavu Ndizi confidence Ohh Yahwe Ndinu mbambande U always here and u never late Mumandipasa phavu Ndizi confidence U deserve all the glory Mbuye wanga ndi one U deserve all the glory Mbuye wanga ndi one Hook Dani wanga amafuna ndiduke Ndiyaluke ndiduke Amafuna ndiduke Ndiyaluke ndiduke Dani wanga amafuna ndiduke Ndiyaluke ndiduke Amafuna ndiduke Ndiyaluke ndiduke Verse Ambuye wanga Mukhale nane mukhale nane Ambuye wanga Mukhale nane mukhale nane I need u Lord please watch over my soul I need u Lord please watch over my soul Afuna nditagwa afuna nditaputwa Afuna nditafa afuna ndingoduwa Pre hook Sindikhala ndimatha Mbuye amandikonda He is always on my side He is always on my side Sindikhala ndimatha Mbuye amandikonda He is always on my side He is always on my side Mbuye wanga kawawa Palibe ofanana naye Iye sanditaya alindicholinga nane Mbuye wanga kawawa Palibe ofanana naye Iye sanditaya alindicholinga nane Hook Dani wanga amafuna ndiduke Ndiyaluke ndiduke Amafuna ndiduke Ndiyaluke ndiduke Dani wanga amafuna ndiduke Ndiyaluke ndiduke Outro Amafuna ndiduke Ndiyaluke ndiduke Afuna nditagwa afuna nditaputwa Afuna nditafa afuna ndingoduwa
Sanatçı: IceKay Malawi
Türü: Belirtilmemiş
Ajans/Yapımcı: Belirtilmemiş
Şarkı Süresi: 3:30
Toplam: kayıtlı şarkı sözü
IceKay Malawi hakkında bilgi girilmemiş.

Fotoğrafı