madah khauya ndiwe bwenzi şarkı sözleri

Mzanga lero kodi uli bwanji Ndikudziwa wagwidwa ndi nthumazi Kuti lero ndili ndi nkhani zanji Ayi usade nkhawa Lero ndangofuna kuti udziwe Chikondi chako nchakuya ngati dziwe Pokondwa polira nzanga ndiiwe Ayi sumandithawa Ndiwe bwenzi Lenileni Ndimakondwera nawe Kupeza iwe Monga nzanga Ayi zedi ndi mdalitso Lingandigwere vuto Uli pompo Nkakondwa ukondwa nane Sindifunanso Nzanga wina Oposa m'mene ulili Pena timatha kusamvetsetsana Kanthawi kochepa tagwirizana Pali zifukwa mazanamazana Chikondi chopanda malire Pena timatha kusamvetsetsana Kanthawi kochepa tagwirizana Pali zifukwa mazanamazana Chikondi chopanda malire Ndiwe bwenzi Lenileni Ndimakondwera nawe Kupeza iwe Monga nzanga Ayi zedi ndi mdalitso Lingandigwere vuto Uli pompo Nkakondwa ukondwa nane Sindifunanso Nzanga wina Oposa m'mene ulili Ndiwe bwenzi Lenileni Ndimakondwera nawe Kupeza iwe Monga nzanga Ayi zedi ndi mdalitso Lingagweee oooh Uhh Ohhhhhh Uhh Kupeza iwe ehh eh Uhh Lingagwe vutoo Pompooo Hah Sindifunansoo ooh Ohhh
Sanatçı: Madah Khauya
Türü: Belirtilmemiş
Ajans/Yapımcı: Belirtilmemiş
Şarkı Süresi: 4:23
Toplam: kayıtlı şarkı sözü
Madah Khauya hakkında bilgi girilmemiş.

Fotoğrafı