madalitso banda vocalist blessings follom me (feat. joe kellz) şarkı sözleri
Blessings will follow me
Blessings will follow me
Will follow me oya- oya -ah
Never been easy nah-nah!
Moyo umawawa uwu yeah
I tell you ndakhalamo, mabvuto ndadutsamo
Koma chaka chino ndikulengeza
Madalitso mbwembwembwe
Zisomo mbwembwembwe
Chaka chino ndi changa
Koma ngati zaka za m'mbuyo ndinkangolira
Koma this year Blessings will follow me
Koma ngati zaka za m'mbuyo ndinkangolira
Koma this year Blessings will follow me
Blessings will follow me (iiiiiii)
Blessings will follow me (iiiiii)
Na chaka chino eh! eh!, eh! eh! eh!
Sindida nkhawa ine eh! eh! eh! eh!
Ndidzingokhala ine phe eh eh eh
Nkhondo amenya nda Ambuye eh! eh! eh!
Chaka cha zisomo, Madalitso momo
Dziko la khwidzi Blessings will follow me still
oooh wo wo oh oh!
Koma ngati zaka za m'mbuyo ndinkangolira
Koma this year Blessings will follow me
Koma ngati zaka za m'mbuyo ndinkangolira
Koma this year Blessings will follow me
Blessings will follow me (iiiiiii)
Blessings will follow me (iiiiii)
Blessings will follow me (iiiiiii)
Blessings will follow me (iiiiii)
Iye eh eh! iye eh! eh!
Follow me, follow me
Follow me, follow me

