madalitso banda vocalist chikondi cha yesu şarkı sözleri
AaaaaHHH! Eyi Eh Eyi EH!
OoooH Omama!! Chindigometsa Chikondi
Chikondi cha Yesu, chikondi cha Yesu
Chikondi cha Yesu ndi chokoma
Chikondi cha Yesu, chikondi cha Yesu
Chikondi cha Yesu ndi chokoma
Anachoka mwamba kusiya ulemelero
Kudzafera ife wabwino Yesu
Chikondi chotere ndani akadaonetsa
Koma Yesu adakondetsetsa ife
Kupereka moyo wake kumvera kuwawa Yesu
Koma Yesu akonda ife eeh- aah
Ngati tili m'fulu leroli alipo anamvera kuwawa
ndim'nkondetsetsa poti iye akonda ifeeee!
Chikondi cha Yesu, chikondi cha Yesu
Chikondi cha Yesu ndi chokoma
Chikondi cha Yesu, chikondi cha Yesu
Chikondi cha Yesu ndi chokoma
Chikondi cha Yesu, chikondi cha Yesu
Chikondi cha Yesu ndi chokoma
Chikondi cha Yesu, chikondi cha Yesu
Chikondi cha Yesu ndi chokoma
Ooh aaah! NDdichokoma, ndichokoma.
Chatipezetsa moyo aah!
Dziko litachimwa Yesu anasiya zonse
Kumwamba Kudzatifera wabwino Yesu
Kulolera kusiya zonse kudzaombola iwe nd'ne
M'bale mvetsera Yesu atikonda
Ah! Yesu koma a Yesuyo, mundikondera chani ine?
Ndimachimwa kulowa njira zosalungama
Koma a Yesu chikondi chanu pa Ine chiyimabe
Chikondi cha Yesu, chikondi cha Yesu
Chikondi cha Yesu ndi chokoma
Chikondi cha Yesu, chikondi cha Yesu
Chikondi cha Yesu ndi chokoma
Chikondi cha Yesu, chikondi cha Yesu
Chikondi cha Yesu ndi chokoma
Chikondi cha Yesu, chikondi cha Yesu
Chikondi cha Yesu ndi chokoma
Chikondi cha Yesu (Chikondano chake)
Chikondi cha Yesu (Chikondano chake)
Chikondi cha Yesu ndi chokoma

