t-no i'm dependent şarkı sözleri

Yeah, hahaha, I feel like Li Wu in this joint.... In the studio preparing to jump on "Pray a lot"... I feel like The Gosple, Aubrey Mvula right before he jumped on "I'ma do it for ya"... I'm feeling blessed y'all! I feel like KB, just when he was about to record "I'ma just do it".... Hahaha, I depend on God bra! yeah! Bet you're wondering why I am feeling like a 100 bucks Jumping up and down all over like a 100 bucks Man i'm feeling like I now can do some summersaults Like an acrobatic man can do some summersaults Ndi Yesu olo n'tagwa ndimagwera m'manja mwake Satana sindim'patsa mita iye sangamake Ndinayisova Yesu ndi yankho checka calculator Opanda ku dalila Yesu ndithu tchimo sungathe kuleka Ndayesa kusiya tchimo ndekha, nzosatheka Ndayesa kuyuza nzeru zanga, nzosatheka Ndayesa kuyuza mphavu zanga, nzosatheka Olo shasha masamba sangathe, nzosatheka Koma ndi Yesu khristu zinthu zimatheka Zinthu zomwe zimavuta kale zimaphweka Im finding life easier and my secret is I lean on Jesus Christ who helps me in my weaknesses (Why you joyous all the time?) I depend on God (Confident you'll make it through) I depend on God (Can't you see no one has done it?) I depend on God (What make's you think you're any different?) I depend on God (Awawa simatama) I'm dependent (Izizi si mphavu zanga) I'm dependent (Opanda Yesu sindingathe) I'm dependent (Ndimadalila Yesu yekha) I'm dependent I'm dependent on God, ndaponda mwala though Tawonani ndachira mutu opanda panado Ok ok, bwino bwino osapanga zanga Koma ndikachira ndimadziwa kuti si mphavu zanga Alipo Yesu amene amachiza ma doctor akalephera 2nd Chronicles 16:12 n'zomwe ikunena Yesu amatha opanda iye ndili chabe ka Ndi mwazi wake okhawo umene ungandichape ka Ndaponda mwala, sindida nkhawa, zanga zinayera I'm dependent on Jehovah osati mayina ena Ena ndi mafano Ena ndi ma fana Ena ndi ma fano ongofuna atafana na I'm depedent on God, ine pa easy basi I never worry bout tomorrow zamudziko basi What I'll eat and what I dress, amapatsa ka Yehova ndi m'busa wanga ndimangophaka pasture ka (Why you joyous all the time?) I depend on God (Confident you'll make it through) I depend on God (Can't you see no one has done it?) I depend on God (What make's you think you're any different?) I depend on God (Awawa simatama) I'm dependent (Izizi si mphavu zanga) I'm dependent (Opanda Yesu sindingathe) I'm dependent (Ndimadalila Yesu yekha) I'm dependent (Why you joyous all the time?) I depend on God (Confident you'll make it through) I depend on God (Can't you see no one has done it?) I depend on God (What make's you think you're any different?) I depend on God (Awawa simatama) I'm dependent (Izizi si mphavu zanga) I'm dependent (Opanda Yesu sindingathe) I'm dependent (Ndimadalila Yesu yekha) I'm dependent
Sanatçı: T-No
Türü: Belirtilmemiş
Ajans/Yapımcı: Belirtilmemiş
Şarkı Süresi: 4:26
Toplam: kayıtlı şarkı sözü
T-No hakkında bilgi girilmemiş.

Fotoğrafı